Malawi Broadcasting Corporation
Local Nkhani

Tajong atha osasewera nawo Blantyre Derby

Katswiri watsopano womwetsa zigoli wa timu ya Mighty Mukuru Wanderers yemwe kwawo ndi ku Cameroon, Sama Thierry Tajong, ndi wokayikitsa ngati asewere nawo Blantyre Derby kaamba koti sanalandilmrebe chilolezo chosewera mpira kapena kugwira ntchito mdziko muno (Work permit) pa chingerezi.

Kumayambiliro kwa sabata ino, Tanjong anasaina mgwirizano wa zaka ziwiri  ndi timu ya Wanderers.

Padakali pano timu-yi ikuyesetsa  kuti katswiri-yu apeze chilolezo chosewera masewero ake woyamba pomwe Wanderers ikukumana ndi timu ya FCB Nyasa Big Bullets masanawa mu ligi ya TNM.

 

Olemba Amin Mussa

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Alimi apeza misika ya ndalama zochuluka kuchiwonetsero chazaulimi

Justin Mkweu

Wanderers, Chitipa answer Airtel’s call with wins

Romeo Umali

Scorchers registers first win at COSAFA

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.