Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News

Sitima ya Marka itha kufika — Chithyola Banda

Sitima yochekera ku Beira m’dziko la Mozambique itha kufika ku Marka m’boma la Nsanje, atero a Chithyola Banda.

Nduna ya zachuma yi yatsindika kuti ntchito yokonza njanji ya sitima kuchoka ku Marka kufika ku Bangula yafika pamapeto, ndipo sitima itha kufika kuchoka ku Beira.

Iwo ayi izi zithandiza kupititsa chuma cha dziko lino patsogolo, maka kupyolera mu ntchito za malonda.

Related posts

Female artists urged to work together

Romeo Umali

HIV AIDs still a threat — DC

Romeo Umali

KAMUZU ACADEMY TO HOST AWARDS FOR NATIONAL MATHS-ENGLISH  COMPETITION

McDonald Chiwayula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.