Malawi Broadcasting Corporation
News Nkhani

President Chakwera akayendera ntchito zachitukuko kumpoto

Mtsogoleri wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, lero anyamuka ku Lilongwe kupita mchigawo chakumpoto kumene akayendere ntchito zina zachitukuko.

Malinga ndi kalata imene wasayinira mlembi wamkulu mu ofesi ya President ndi  nduna zake, a Colleen Zamba, mwazina Dr Chakwera akakhala nawo pamwambo watsiku lokumbukira anthu amene adadzipereka kuti dziko lino likhale pa ufulu (Martyrs Day).

Mwambowu umakhalapo pa 3 March chaka chilichonse ndipo chaka chino tsikuli likhala pa lamulungu (Sunday).

Related posts

Voting commences in the UTM elective convention

MBC Online

Kamtukule urges MSE to boost ownership shares awareness

Rabson Kondowe

Khulubvi Arts and Cultural Festival yafika pa mpondachimera

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.