Malawi Broadcasting Corporation
Africa Crime Local Local News Nkhani Politics

“Osanyoza anthu achikulire” — Chakwera

President Lazarus Chakwera wati khalidwe lonyoza anthu achikulire powanena kuti ndi mfiti ndi kuwapha (mob justice) zili ndi kuthekera kosokoneza ana achichepere m’dziko muno.

A Chakwera ati ndi pofunikanso kukhala ogwirizana, posatengera kusiyana zipani, zipembedzo ndi zina zambiri popeza anthu akakhala ogwirizana, dziko lino likhoza kupambana nkhondo yolimbana ndi njala.

#ChakweraDevelopmentalRally

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Zomba communities awarded land certificates

Timothy Kateta

MP urges churches to combat rising suicide cases

Sothini Ndazi

Former Nkhoma Synod Secretary General inaugurated as Group Gusu

Paul Mlowoka
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.