Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani Sports Sports

Mzimba Stadium yatsala pang’ono kutha

Adindo a khonsolo ya Mbelwa ati ntchito yomanga bwalo la masewero la Mzimba ikhala ikufika kumapeto pofika m’mwezi wa December chaka chino.

M’modzi mwa akulu akulu a khonsoloyi, a Allan Chitete, ati zambiri zofunikira pa bwalori zinatheka kale.

Bwalo limeneli ndi lokwana anthu 25, 000 ndipo lidzakhalanso ndi ma ofesi amene khonsoloyi idzidzachitira malonda.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Two in cooler for selling counterfeit fertilizer

Romeo Umali

Utilise irrigation to contain drought-induced hunger – Agriculturalist

Sothini Ndazi

Government launches National Development Policy to bolster self-reliance, sustainability

McDonald Chiwayula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.