Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

Mwambo wa chikumbutso wayamba ku Mulanje

Mneneri Shepherd Bushiri ndi mmodzi wa atsogoleri azipembedzo omwe afika ku Mulanje, komwe mwambo wachikumbutso Cha Namondwe Freddy ukuchitikira.

Bushiri wakhala akuthandiza anthu okhudzidwa ndi Namondweyu munjira zosiyanasiyana monga chakudya, ndalama mwazina.

Masabata apitawa, iye anayamikira boma pomulola kugawa chakudya komanso kutenga nawo gawo pa chitukuko cha dziko lino.

Olemba: Blessings Cheleuka
#MBCOnlineServices

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Court to deliver verdict on bus depots case in September

MBC Online

Moyale Barracks thumps CIVO

Rudovicko Nyirenda

Police launch investigation on Zolozolo church fracas

Rudovicko Nyirenda
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.