Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

Mwambo wa chikumbutso wayamba ku Mulanje

Mneneri Shepherd Bushiri ndi mmodzi wa atsogoleri azipembedzo omwe afika ku Mulanje, komwe mwambo wachikumbutso Cha Namondwe Freddy ukuchitikira.

Bushiri wakhala akuthandiza anthu okhudzidwa ndi Namondweyu munjira zosiyanasiyana monga chakudya, ndalama mwazina.

Masabata apitawa, iye anayamikira boma pomulola kugawa chakudya komanso kutenga nawo gawo pa chitukuko cha dziko lino.

Olemba: Blessings Cheleuka
#MBCOnlineServices

Related posts

Standard Bank empowers girls through financial literacy

Rabson Kondowe

Summit a platform to highlight challenges — Chakwera

Rabson Kondowe

VETERAN POLITICIAN MWAMBUNGU DIES

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.