Malawi Broadcasting Corporation
Local News Nkhani

Mtukula pakhomo ndi popumira — Sendeza

Nduna yoona kuti pasamakhale kusiyana pantchito pakati pa amuna ndi akazi, a Jean Sendeza, ati kukhazikitsidwa kwa mtukula pakhomo wa m’mizinda ndi chitsimikizo choti mtsogoleri wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, wadzipereka kuonetsetsa kuti anthu apeze popumira pamene boma likukonza chuma cha dziko lino.

Mai Sendeza anena izi ku Zomba kumene ntchito yokhazikitsa mtukula pakhomo wa m’mizinda ya K15.7 billion ili mkati.

Iwo apempha anthu omwe akusankha opindula kuti asamakondere palembana maina.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Fines imposed for illegal tree cutting in Balaka

Romeo Umali

“A Gotani – Hara ali ndi luntha potsogolera” — President Chakwera

Timothy Kateta

Apostle Kawinga aids hunger stricken families in CK

Jeffrey Chinawa
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.