Malawi Broadcasting Corporation
Local News Nkhani

Mtukula pakhomo ndi popumira — Sendeza

Nduna yoona kuti pasamakhale kusiyana pantchito pakati pa amuna ndi akazi, a Jean Sendeza, ati kukhazikitsidwa kwa mtukula pakhomo wa m’mizinda ndi chitsimikizo choti mtsogoleri wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, wadzipereka kuonetsetsa kuti anthu apeze popumira pamene boma likukonza chuma cha dziko lino.

Mai Sendeza anena izi ku Zomba kumene ntchito yokhazikitsa mtukula pakhomo wa m’mizinda ya K15.7 billion ili mkati.

Iwo apempha anthu omwe akusankha opindula kuti asamakondere palembana maina.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Malawi to benefit from €5.5 bn Italian funding to Africa

Blessings Kanache

‘Malamulo a chipani akuvomereza atosgoleri ake kudzachita mgwirizano ndizipani zina’

Yamikani Simutowe

Tobacco fetches almost K5,000 per Kg on market opening day

Trust Ofesi
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.