Malawi Broadcasting Corporation
Business Development Local Local News

Mtengo wa Chocolate utha kukwera

Pali nkhawa kuti kuchepa kwa mlingo wa cocoa yemwe amalimidwa m’maiko amene ali kuchigawo cha kumadzulo kwa Africa kupangitsa kuti mitengo ya chokoleti padziko lonse ikwere.

Maiko a Ghana ndi Ivory Coast amalima 60% ya cocoa pa dziko lonse, ndipo maiko awiriwa akhala akukumana ndi mavuto pa ulimiwu.

Malipoti akuti m’dziko la Ghana, minda yoposa 590,000 hectares ya cocoa yakhudzidwa ndi nthenda yotchedwa “swollen foot” yomwe imayamba kaye yachepetsa zokolola, isanapheletu mitengo ya cocoa.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Junior Queens have a bright future — Chakwera

Romeo Umali

Bullets is confident — Pasuwa

MBC Online

Chitimba Communities demand action on delayed Water Supply Project

Rudovicko Nyirenda
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.