Malawi Broadcasting Corporation
Business Development Local Local News

Mtengo wa Chocolate utha kukwera

Pali nkhawa kuti kuchepa kwa mlingo wa cocoa yemwe amalimidwa m’maiko amene ali kuchigawo cha kumadzulo kwa Africa kupangitsa kuti mitengo ya chokoleti padziko lonse ikwere.

Maiko a Ghana ndi Ivory Coast amalima 60% ya cocoa pa dziko lonse, ndipo maiko awiriwa akhala akukumana ndi mavuto pa ulimiwu.

Malipoti akuti m’dziko la Ghana, minda yoposa 590,000 hectares ya cocoa yakhudzidwa ndi nthenda yotchedwa “swollen foot” yomwe imayamba kaye yachepetsa zokolola, isanapheletu mitengo ya cocoa.

Related posts

Apolisi abalalitsa anthu omwe amachita zipolowe pa mpingo wa CCAP wa Mibawa ku Mbayani

Romeo Umali

Malawi will face South Africa in COSAFA Beach Soccer opener

Romeo Umali

Yamal, Rodrigo honoured at Euro 2024 awards

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.