Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

Mphamvu ya Kwacha yakhazikika

Ndalama ya Kwacha yakhazikikabe pa mtengo wa K1751 pogula ndalama ya Dollar imodzi pomwe inafika mu March chaka chino.

Izi ndi malinga ndi msika wa ndalama zakunja omwe banki ya Reserve inachititsa lachinayi sabata yatha omwe banki zisanu zinachita nawo.

Ndalamayi ikuyembekezeka kupitilira kukhazikika pamene ndalama zakunja zochokera ku fodya pano zakwana $182 million (pafupifupi K318 billion).

Related posts

‘Anthu opitilira 3,000 amwalira kaamba ka vuto la mpima’

Rabson Kondowe

Madam Chakwera apempha mafumu kuti alimbikitse ana pa maphunziro

Rabson Kondowe

‘Mgwirizano ndi ofunika pa ntchito yobwezeretsa chilengedwe’

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.