Malawi Broadcasting Corporation
Local News Nkhani

MNENERI BUSHIRI WAGAWA CHIMANGA KU THYOLO

Prophet Shepherd Bushiri wagawa chimanga kwa Nchilamwera m’boma la Thyolo komwe wapempha anthu kuti asalowetse ndale pa thandizo lake.

Mneneri Bushiri wati apitirizabe kupereka chimanga kwa anthu okhudzika ndi njala m’madera onse m’dziko muno, pomwe mabanja oposa 40,000 tsopano alandira chimangacho.

Mneneriyu wapemphanso amfumu a Nchilamwera kuti adziwitse a khonsolo ya bomali kuti ngati angamulole, athandize pantchito yomanga technical college pa boma la Thyolo.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

CHAKWERA TO ATTEND SEVENTH DAY ADVENTIST BLANTYRE CENTENARY CELEBRATIONS

McDonald Chiwayula

MBC HAILS TIES WITH CHINESE EMBASSY

McDonald Chiwayula

District councils urged to enforce spatial plans for development

Austin Fukula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.