Malawi Broadcasting Corporation
Agriculture Business Development Local News Nkhani

Malawi yapeza $2 million kuchokera ku Israel

Photo Credit : Gianluigi Guercia

Pofika mwezi uno, dziko la Malawi lapeza ndalama zokwana $2 million (pafupifupi K3.4 billion) kuchoka ku ndondomeko yotumiza achinyamata kukagwira ntchito mu dziko la Israel.

Izi ndi malingana ndi nduna yowona zachuma, a Simplex Chithyola Banda.

A Chithyola Banda ati pakutha pa mwezi uno, akuyembekezera kuti dziko lino likhala litapeza $1 million (pafupifupi K1.7 billion) yowonjezera.

Iwo ati izi zikuthandiza dziko lino kumbali yopeza ndalama zakunja mosavuta.

Related posts

Young scorchers back home for second leg

Romeo Umali

Mthunzi Funeral Services open new centre in Lilongwe

Yamikani Simtowe

ZAMBIRI MWA ZIMENE A CHAKWERA ANALONJEZA MU SONA YA 2023 ZACHITIKA – NDUNA

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.