Malawi Broadcasting Corporation
Agriculture Business Development Local News Nkhani

Malawi yapeza $2 million kuchokera ku Israel

Photo Credit : Gianluigi Guercia

Pofika mwezi uno, dziko la Malawi lapeza ndalama zokwana $2 million (pafupifupi K3.4 billion) kuchoka ku ndondomeko yotumiza achinyamata kukagwira ntchito mu dziko la Israel.

Izi ndi malingana ndi nduna yowona zachuma, a Simplex Chithyola Banda.

A Chithyola Banda ati pakutha pa mwezi uno, akuyembekezera kuti dziko lino likhala litapeza $1 million (pafupifupi K1.7 billion) yowonjezera.

Iwo ati izi zikuthandiza dziko lino kumbali yopeza ndalama zakunja mosavuta.

Related posts

Smiles in Dedza as Hilal Afrika donates boreholes

MBC Online

ANC to form coalition Government as no party secures majority

Romeo Umali

Phindu la Illovo latsika mu miyezi isanu ndi umodzi

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.