Malawi Broadcasting Corporation
News Nkhani

Ma Banki apeza phindu lochuluka

Ma Banki asanu ndi atatu a m’dziko muno apanga phindu lokwana K256.7 billion m’chaka cha 2023 chokha, boma litadulapo kale msonkho.

Izi ndi malingana ndi lipoti la m’mene chuma chikuyendera m’dziko muno lochokera ku banki yayikulu pa dziko lonse (World Bank).

Lipotili lati phinduli lakwera kuchoka pa K170.8 billion lowe ma banki-wa anapeza m’chaka cha 2022.

Bankiyi yati ngakhale chuma cha dziko lino chakumana ndi mavuto ambiri, gawo la mabanki likupitilira kukwera komanso kupeza  phindu lochuluka.

Related posts

Bungwe la CARD lati MBC ndi akadaulo powulutsa mawu

Romeo Umali

CHAPONDA FAILS TO ATTEND PARLIAMENTARY BUSINESS COMMITTEE MEETING

MBC Online

Matola hails arrival of 51 million litres of fuel as game-changer

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.