Mbusa amenyana ndi mlembi kamba ka malo
M’busa wa mpingo wina ku Tsangano m’boma la Ntcheu akuti wamenyana koopsya ndi mlembi wake wa mpingowu chifukwa chokanganila malo.
Atumizilidwa njoka kamba koyenda ndi mayi wapabanja
Mnyamata wina ogulitsa nyama ya mbudzi pa msika wina kwa mfumu Mtwalo mboma la Mzimba wathawa pa malo pake pa bizinesi mwamuna wa mkazi yemwe anali naye pa chibwenzi atatumiza njoka ya masenga kuti ithane ndi mkuluyo pa malopo.
Mayi wina athawisana ndi ogulisa fodya
Anthu okhala ku Bilila m’boma la Ntcheu ati akudabwa ndi zomwe wachita mai wina posiya mwamuna wake yemwe anaberekerana naye ana asanu ndikuthawisana ndi mnyamata wina yemwe amakugula fodya mderalo.
Mphongo ziwiri zikunthana mpaka kuchosana mano
Amuna awili anakunthana kodetsa nkhawa mpaka kuchotsana mano pamudzi wina kwa Che Somba mboma la Blantyre.