30
August

30/08/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 3633 times

Mwamuna wina atandala mnyuma kamba ka manyazi

Mwamuna wina mdera la Mazengera m’boma la Lilongwe akukhalira kutandala mnyumba chifukwa cha manyazi ndi zomwe zamuchitikira.

29
August

29/08/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 2294 times

Katswili oyimba za uzimu achita manyazi
M’modzi mwa akatswili oimba nyimbo za uzimu ku Blantyre akuyenda wela-wela ngati nkhuku yogwela mvuwo chifukwa cha manyazi.

24
August

24/08/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 2299 times

Anthu aku Lilongwe akhala mwa mantha
Anthu a mdera la Senior Group Malembe kwa Chitukula mboma la Lilongwe akukhala mwa mantha.

23
August

23/08/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 2624 times

Mai wina atandala mnyumba kamba ka manyazi

Mai wina akukhalira kutandala mnyumba kwa Changoima mdera la Chapananga m’boma la Chikwawa chifukwa cha manyazi.

Get Your Newsletter