21
April

20/04/15

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 3897 times

Azindikira kuti akudyetsedwa konda ine

Mwamuna wina wakwa Zinganguwo ku Sigelege mu mzinda wa Blantyre akuyenda ali khuma khuma, kudandaula atatulukira kuti mkazi wake adamudyetsa kondaine.

21
April

19/04/15

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 3448 times

Chipwilikiti pa maliro 

Kunali chipwilikiti pa maliro ena omwe anachitika m’mudzi wina kwa T/A Chadza mboma la Lilongwe pamene adzukulu anasemphana maganizo ndi Mfumu ya m’mudzimo.

17
April

17/04/15

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 3529 times

Sing’anga agonana ndi mayi pochosa matsoka
Anthu a mdera lina mboma la Blantyre ati ndiokhumudwa kwambiri ndi zomwe anachita Sing’anga wina powumiliza kugonana ndi mayi wina ati pofuna kumuchotsa matsoka omwe akhala akukakamira mayiyo komanso ndikumuuza kuti agonanenso ndi mwamuna wake akuonerela.

16
April

16/04/15

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 3581 times

Awona polekera kuchita zachimasomaso
Bambo wina wachimasomaso kwa T/A Chimombo mboma la Nsanje aona polekera atagonana ndi mtsikana yemwe bamboyo amayembekezera kuti aperekeze mdzukulu wake pokafunsila ukwati.

Get Your Newsletter