Agonana ndi ana awo awirir owapeza
Anthu a m’mudzi wa Malunga Mfumu yayikulu Mponda m’boma la Mangochi ati ndiwokhumudwa kwambiri komanso odana nkhawa ndi zomwe akhala akuchita bamboo wina pogonana ndi ana ake awiri owapeza kwa nthawi yayitali.
Mkazi wa nyakwawa awilikiza chimasomaso
Mkazi wa Nyakwawa wina mdera la Chakhadza m’boma la Lilongwe wakhumudwitsa anthu chifukwa cha khalidwe lake lachimasomaso.
Athesa banja atanamizidwa zaukwati wina
Mayi wina wa mdera la Mfumu Mkanda m’boma la Mchinji manja ali mkhosi atapasula banja lake pomvera mwamuna wina yemwe anamunamiza kuti amukwatira.
Mbusa wamkazi afunsira mlembi wa mpingo
Anthu a mpingo wina ku Nathenje mboma la Lilongwe aleka kupita ku kachisi zitadziwka kuti mbusa wao yemwe ndi wa mkazi amafunsila mlembi wake yemwe ndi wa mwamuna.