Mai wina achimina ku Mulanje
Mai wina wachimina ku Mwanamulanje mdera la Chambe m’boma la Mulanje.
Azitsekera mnyumba kuopa zibagera
Mwamuna wina mdera la Chikowi m’boma la Zomba zinamukoka manja atazitsekera mnyumba kuopa zibagera zochokera kwa mkazi wake.
Alandidwa maliro
Ana a banja lina m’boma la Thyolo anagwira njakata atawalanda maliro a atate awo pa chipatala china m’boma la Blantyre.
Anamiza mamuna kuti ali ndi pathupi
Mai wina kwa Ndakwera mboma la Chikwawa amuthamangitsa pa ukwati zitadziwika kuti amanamiza mwamuna wake kuti ali ndi pathupi.