08
September

08/09/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 3894 times

Mai wina achimina ku Mulanje

Mai wina wachimina ku Mwanamulanje mdera la Chambe m’boma la Mulanje.

07
September

07/09/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 3528 times

Azitsekera mnyumba kuopa zibagera

Mwamuna wina mdera la Chikowi m’boma la Zomba zinamukoka manja atazitsekera mnyumba kuopa zibagera  zochokera  kwa mkazi wake.

01
September

01/09/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 4449 times

Alandidwa maliro
Ana a banja lina m’boma la Thyolo anagwira njakata atawalanda maliro a atate awo pa chipatala china m’boma la Blantyre.

31
August

31/08/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 2560 times

Anamiza mamuna kuti ali ndi pathupi

Mai wina kwa Ndakwera mboma la Chikwawa amuthamangitsa pa ukwati zitadziwika kuti amanamiza mwamuna wake kuti ali ndi pathupi.

Get Your Newsletter