26
May

22/05/15

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 2791 times

Ayenda mwamanyazi mbiri yawo itawanda
Mnyamata wina kwa Iwala ku Ntaja m’boma la Machinga akuyenda zamadulira atazindikira kuti mbiri yake yawanda yofuna kulanda katundu wa m’nyumba ya mchemwali wake.

21
May

21/05/15

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 3044 times

Mbava itupa mimba kamba kokuba mbuzi
Mbava ina kwa Mbera m’boma la Balaka ili pa ululu woopsya itatupa mimba chifukwa chakuba mbuzi ya mai wina mderalo.

21
May

20/05/15

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 2681 times

Ukwati utha kamba ka chimasomaso
Mayi wina kwa Kanduku mboma la Mwanza akunong’oneza bondo mwamuna wake atamuuza kuti ukwati watha chifukwa cha khalidwe lake la chimasomaso.

19
May

19/05/15

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 3103 times

Mayi okonda zopemphera agwidwa akuchita zadama
Mayi wina wodziwika bwino ndi nkhani zopemphera ku Urongwe mboma la Balaka wakhumudwitsa anthu atagwidwa akuchita zachisembwere kunja kutachita kachisisila chakumadzulo  mtchalichi ina yomwe iye sapempherako.

Get Your Newsletter