29
May

26/06/15

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 2947 times

Banja lisokonekela kamba ka kovinisa

Banja lina latekeseka m’dera la Mfumu Mkanda mboma la Mulanje mkulu wina atapeza mkazi wake akuvina ndi mphongo zina m’mudzimo.

29
May

25/05/15

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 2725 times

Agwira nchiuno mwa munthu odwala

Anthu a m’mudzi mwa Likhonyowa  mboma la Machinga anatsala pang’ono kuthidzimula mkulu wina atamuzindikira kuti amagwira nchiuno mwa munthu odwala.

27
May

24/05/15

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 2879 times

Athyole nthumba ndalama ya eni
Mkulu wina akuyenda mogwetsa nkhope yake pansi chifukwa cha manyazi mu mzinda wa Blantyre atamtulukila kuti anathyolela mthumba ndalama yomwe anamupatsa kuti akasiye ku banki.

27
May

23/05/15

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 3162 times

Akuluakulu ena apita kumanda kufuna chakudya
Nyakwawa ina ku Chilomoni mu mzinda wa Blantyre yachenjeza adzukulu omwe akumakonda kupita kumanda akaona kuti chakudya chayandikila basi.

Get Your Newsletter