10
June

07/06/15

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 2566 times

Azimayi atatu awilikiza uhule
Anthu aku Mbayani mu mzinda wa Blantyre akuti aimika manja m’mwamba chifukwa cha zomwe amai atatu apa banja akuchita powilikiza za uhule ndi amuna apa banjanso.

10
June

06/06/15

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 2469 times

Akolola chimanga cha eni
Anyamata ena awiri kwa Kwataine m’boma la Ntcheu awakwidzinga atawagwira akukolola chimanga m’munda wa mwini.

05
June

05/06/15

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 3097 times

Akuchimuna akana kupita kuukwati
Makolo a mnyamata wina ku Misesa kwa Kapeni mboma la Blantyre amenyetsa nkhwangwa pa mwala kuti sadzapita ku ukwati wapa tchalitchi wa mwana wao wa mwamuna kumapeto a mwezi uno chifukwa choti akuchikazi akuyendetsa okha zokonzekera zonse za chisangalalo-cho.

04
June

04/06/15

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 2771 times

Mtsikana oyendayenda atibulidwa pamaliro
Mtsikana wina oyendayenda m’mudzi wa Kapichi m’boma la Thyolo amutibula mpaka kukomoka pa mwambo wamaliro.

Get Your Newsletter