14
September

14/09/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 3164 times

Banja lithela ku malo ogonela alendo

Mai wina ku Malimba pa boma la Salima manja ali ku nkhongo banja lake litathera ku malo ogona alendo.

12
September

12/09/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 2299 times

Mai wina alodzedwa dzala

Mai wina yemwe amatsogolera ntchito za kumpingo wina akumuloza chala pa zomwe wachita kwa gulupu Likhomo mdera la  mfumu M’biza m’boma la Zomba.

11
September

11/09/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 2457 times

Mwamuna wina manja ali kunkhongo banja litatha
Mwamuna wina ku Lunzu mu mzinda wa Blantyre manja ali ku nkhongo banja lake litakathera kubwalo la nyakwawa.

10
September

10/09/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 4107 times

Mtsikana wina ali m'manja mwa a polisi

Mtsikana wina ali mmanja mwa a polisi kwa gulupu Namalima mdera la Senior Authority Ngwerero m’boma la Zomba.

Page 14 of 147

Get Your Newsletter