Anthu akwiya ndi nduna ina ku Chikwawa
Anthu okhala mdera la Ndakwera m’boma la Chikwawa ati ndi okwiya ndi zomwe yachita nduna ya mfumu ina pomwe inapita kukaveka unyakwawa.
Akangana ndi mkazi wake kamba ka bulu
Tili mboma la Lilongwe m’mudzi mwa Nyundo kwa T/A Chadza mwamuna wina wakangana kwambili ndi mkazi wake pa nkhani ya bulu.
Anjatidwa kamba kogwilira mwana wa zaka khumi
Mwamuna wina wa zaka makumi awiri m’dera la Mfumu Liwonde mboma la Machinga amulamula kuti akakhale ku ndende zaka khumi nzinayi chifukwa chogwilira mulamu wake wa zaka khumi.
Amugwilira njoka yake yokawa ndalama
Mkulu wina kwa Mfumu Njolomole mboma la Ntcheu mwina akhoza kulowa m’ntchire, munthu wina atamugwilira njoka yake yomwe imamuthandiza pokawa ndalama za anthu m’deralo.