02
October

02/10/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 3654 times

Anthu akwiya ndi nduna ina ku Chikwawa

Anthu okhala mdera la Ndakwera m’boma la Chikwawa ati ndi okwiya ndi zomwe yachita nduna ya mfumu ina pomwe inapita kukaveka unyakwawa.

29
September

29/09/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 3981 times

Akangana ndi mkazi wake kamba ka bulu

Tili mboma la Lilongwe m’mudzi mwa Nyundo kwa T/A Chadza mwamuna wina wakangana kwambili ndi mkazi wake pa nkhani ya bulu. 

28
September

28/09/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 3620 times

Anjatidwa kamba kogwilira mwana wa zaka khumi
Mwamuna wina wa zaka makumi awiri m’dera la Mfumu Liwonde mboma la Machinga amulamula kuti akakhale ku ndende zaka khumi nzinayi chifukwa chogwilira mulamu wake wa zaka khumi.

27
September

27/09/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 3475 times

Amugwilira njoka yake yokawa ndalama

Mkulu wina kwa Mfumu Njolomole mboma la Ntcheu mwina akhoza kulowa m’ntchire, munthu wina atamugwilira njoka yake yomwe imamuthandiza pokawa ndalama za anthu m’deralo.

Page 12 of 147

Get Your Newsletter