09
October

09/10/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 2787 times

Mai wina adabwisa anthu ndi khalidwe lake

Mai wapa mudzi wina kwa Chikowi m’boma la Zomba akudabwitsa anthu kamba ka khalidwe lake.

07
October

07/10/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 4901 times

Mwamuna wina adabwitsa anthu pa maliro
Mwamuna wina pa mudzi wina kwa Kachere m’boma la Dedza wadabwitsa anthu pa maliro a mwana wake.

04
October

04/10/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 4793 times

Anyanyalilidwa mwana ku ntchito

Mwamuna wina yemwe amagwira ntchito ku bungwe lina kwa Chimwaye kwa Kwataine m’boma la Ntcheu anazingwa mkazi wake atamunyanyalira mwana wa miyezi itatu ku ntchito.

03
October

03/101/7

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 3249 times

Bambo wina amuminitsa ku Lilongwe

Bambo wina yemwe wakhala akunyozera kupita ku maliro a nzake amuminitsa ku Area 49 mu mzinda wa Lilongwe.

Page 11 of 147

Get Your Newsletter