13
April

11/04/15

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 4123 times

Njonda ina iba mabelo afodya
Njonda ina ya m’mudzi mwa Bwananyambi m’boma la Mangochi yathawa anthu ataituluki kuti inaba mabelo a fodya kwa mu mlimi wina.

13
April

10/04/15

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 4272 times

Apasula banja kamba kachimasomaso
Mayi wapa mudzi wina m’dera la mfumu Symon m’boma la Neno wapasula banja ndi manja ake kamba ka khalidwe lake lachimaso-maso.

13
April

09/04/15

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 4426 times

Nkhandwe likolowola maso amkulu wina
Mwamuna wapa mudzi wina kwa Mazengera m’boma la Lilongwe ali mu ululu woopsya nkhandwe itamukolowola maso usiku ataledzera.

10
April

07/04/15

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 4937 times

Anyamula maliro pa kaliyala
Mikoko yogona yapa mudzi wina ku Mtunthama mboma la Kasungu yaima mitu ndi zomwe wachita m’nyamata wina ponyamula malilo abambo ake pa kaliyala ya Njinga ya moto.Nkhani-yi ikuti m’nyamatayo ali ndi golosale ndipo masiku apitawa wakhala akuyenda ndi mkulu wina wa zitsamba pamene bambo ake amadwala mchipatala.

Page 147 of 147

Get Your Newsletter