Mai wina ku Blantyre akuyenda mogwetsa nkhope yake pansi chifukwa cha manyazi.
Mtengwa wina mdera la Kacheche ku Mzimba ati sakumvetsa ndi zomwe zamuchitikira.
Banja lina ndi nyakwawa ina mdera la Malili ku Lilongwe akuyang’anizana ndi diso la mkhwezule.
Mai wina ku Blantyre akuyenda mogwetsa nkhope yake pansi chifukwa cha manyazi.