21
December

21/12/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 4161 times

Omvera paja pali mau oti magwiragwira amapha manja. Nkhaniyi yapherezera mdera la Mzukuzuku ku Mzimba pamene mnyamata wina wayamba kulankhula zosamveka atakaba mtondo wapa banja lina.

17
December

17/12/18

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 5192 times

Mwamuna wina kwa Ganya m’boma la Ntcheu zamusokonekera mkazi wa chibwezi atamulanda foni.

13
December

13/12/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 4714 times

Mwamuna wina ku Migowi m’boma la Phalombe yemwe anali pa ubwenzi wa ntseri ndi mkazi wamwini wachimina.

12
December

12/12/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 4293 times


Ntchembere zina ku Fatima m’dera la mfumu Mlolo m’boma la Nsanje zinakalipira mai wina wa mwana m’modzi poyankhula zoduka mutu pagulu.

Page 4 of 147

Get Your Newsletter