You are here:CategoriesNkhani Zam'maboma
14
June

14/06/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 2969 times

 

Mkulu wina afufuma nkhope ngati chitumbuwa

Mkulu wina wapa mudzi wa Bazirio m’boma la Mchinji akubindikira m’nyumba kamba ka manyazi nkhope yake itafufuma monga chitumbuwa.

13
June

13/06/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 4937 times

Mnyamata wina aba kabudula wachikazi musitolo

M’nyamata wina wa kabaza wapa mudzi wa Chipakuza ku Nchalo m’boma la Chikwawa watha masiku angapo asakupita ku geni yake mbiri itawanda kuti anamugwira akuba kabudula wa mkati m’sitolo ina yotchuka kumeneko.

12
June

12/06/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 2616 times

Dalaivala ayenda zamadulira atagulisa engine 
Dalaivala wina ku Chilomoni mu mzinda wa Blantyre akuti wathawa ndipo akungoyendayenda mtchire powopa achitetezo omwe akumufunafuna pomuganizira kuti agulitsa engine ya galimoto yomwe amayendera.

09
June

09/06/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 7071 times

Gogo wina auka kwa akufa
Anthu akwa Gunda mdera la Jenala ku Phalombe akukhala mwa mantha chifukwa cha zomwe zawachitikira.

About us

Malawi Broadcasting Corporation is a public broadcaster mandated and formed by Government under an Act of Parliament in 1964, to enhance the successful implementation of all its social and economic programs...

Social Media

Catch us on these social networks for more information

Facebook Twitter RSS

Get Your Newsletter