Athawa kuntchito kamba ka ngongole
Mkulu wina wathawa ku ntchito kwake chifukwa cha ngongole mdera la Kapoka m’boma la Chitipa.
Apasula banja yekha
Mkazi wina ku Bwanje m’boma la Ntcheu manja ali ku nkhongo atapasula banja lake ndi manja ake.
Abindikila kamba ka manyazi
Mwamuna wina wochita bizinezi ya golosale ku Chikangawa m’boma la Mzimba akukhalira kubindikira nyumba chifukwa cha manyazi.
Malonda asokonekela
Malonda anatsokonekera masanawu pa msika wa Namphungo mdera la Mfumu Juma m’boma la Maulanje. Yemwe watumiza nkhaniyi wati pamalopo pali banja lina lomwe mai wabanjalo ndi wolimbikira kuchita malonda pofuna kudzipezera zosowa pamoyo wake.