You are here:CategoriesNkhani Zam'maboma
13
July

13/07/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 4113 times

Athawa kuntchito kamba ka ngongole

Mkulu wina wathawa ku ntchito kwake chifukwa cha ngongole mdera la Kapoka m’boma la Chitipa.

11
July

11/07/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 3427 times

Apasula banja yekha

Mkazi wina ku Bwanje m’boma la Ntcheu manja ali ku nkhongo atapasula banja lake ndi manja ake.

10
July

10/07/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 1484 times

Abindikila kamba ka manyazi
Mwamuna wina wochita bizinezi ya golosale ku Chikangawa m’boma la Mzimba akukhalira kubindikira nyumba chifukwa cha manyazi.

07
July

07/07/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 1639 times

Malonda asokonekela

Malonda anatsokonekera masanawu pa msika wa Namphungo mdera la Mfumu Juma m’boma la Maulanje. Yemwe watumiza nkhaniyi wati pamalopo pali banja lina lomwe mai wabanjalo ndi wolimbikira kuchita malonda pofuna kudzipezera zosowa pamoyo wake.

About us

Malawi Broadcasting Corporation is a public broadcaster mandated and formed by Government under an Act of Parliament in 1964, to enhance the successful implementation of all its social and economic programs...

Social Media

Catch us on these social networks for more information

Facebook Twitter RSS

Get Your Newsletter