Anthu ada nkhawa ndi zochita za mnyamata wina
Anthu a mdera la Chakhumbira mboma la Ntcheu ati akuda nkhawa ndi zomwe akuchita mwamuna wina mderalo.
Mai wina abindikila kamba ka ngongole
Mai wina ku Likoma akukhalira kubisala chifukwa cha ngongole. Nkhaniyi ikuti maiyo zaka ziwiri zapitazo analowa mgulu losungitsa ndi kubwereketsana ndalama ya banki nkhonde.
Mai wina odziwika ndi zauzimu achita manyazi
Mai wina wodziwika bwino pa nkhani za Ambuye kwa Kaphuka ku dedza akuyenda njira zodula chifukwa cha manyazi.
Mwamuna wa bizinesi abindikila mnyumba
Mwamuna wina wochita bizinezi ya golosale ku Chikangawa m’boma la Mzimba akukhalira kubindikira nyumba chifukwa cha manyazi.