You are here:CategoriesNkhani Zam'maboma
01
August

01/08/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 2001 times

Mwini mbumba adabwitsa anthu
Tili m’dera la mfumu Chimaliro m’boma la Thyolo, mwini mbumba wina wadabwitsa anthu kumeneko.

28
July

28/07/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 5551 times

Athamangitsa mayi ake kamba ka malo

Mikoko yogona ku Manyowe m’boma la Blantyre yapukusa mitu kamba ka zomwe akuchita nmyamata wina pothamangiza mai ake kamba ka malo.

27
July

27/07/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 1848 times

Banja litha atamenya mamuna kumalo obisika
Mai wina ku Zalewa manja ali ku nkhongo kamba koti banja lake latha atamenya mwamuna wake ku malo obisika.

26
July

26/07/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 1438 times

Mkulu wina yemwe ndi msodzi ku Lumbaulu m’dziko la Mozambiki waopsyeza kuti athana ndi munthu aliyense yemwe wamudyera nsima yake ya ndiwo nsomba.

About us

Malawi Broadcasting Corporation is a public broadcaster mandated and formed by Government under an Act of Parliament in 1964, to enhance the successful implementation of all its social and economic programs...

Social Media

Catch us on these social networks for more information

Facebook Twitter RSS

Get Your Newsletter