Mwini mbumba adabwitsa anthu
Tili m’dera la mfumu Chimaliro m’boma la Thyolo, mwini mbumba wina wadabwitsa anthu kumeneko.
Athamangitsa mayi ake kamba ka malo
Mikoko yogona ku Manyowe m’boma la Blantyre yapukusa mitu kamba ka zomwe akuchita nmyamata wina pothamangiza mai ake kamba ka malo.
Banja litha atamenya mamuna kumalo obisika
Mai wina ku Zalewa manja ali ku nkhongo kamba koti banja lake latha atamenya mwamuna wake ku malo obisika.
Mkulu wina yemwe ndi msodzi ku Lumbaulu m’dziko la Mozambiki waopsyeza kuti athana ndi munthu aliyense yemwe wamudyera nsima yake ya ndiwo nsomba.