Mkulu wina abindikila mnyumba kamba ka manyazi
Mkulu wina yemwe akumuganizila kuti ndi mbala yothelatu kwa Mchinguza kufupi ndiku Nayuchi mboma la Machinga akubindila m’nyumba chifukwa cha manyazi.
Zilombo zilipila mbuzi kamba kolowa mtchalitchi
Zilombo ziwiri za gule wamkulu kwa Chakhadza mboma la Dowa azilipilitsa mbuzi imodzi chilichonse chifukwa cholowa mtchalitchi cha mpingo wina m’deralo.
Atandala mnyumba kamba ka manyazi
Mwamuna wina yemwe ndi mwini nyumba zina zochititsa lendi ku Ndirande mu mzinda wa Blantyre akukhalira kutandala mnyumba chifukwa cha manyazi.
Banja lina liweyeseka ku Machinga
Banja lina pa mudzi wa Kumbalangwe kwa Nkula m’boma la Machinga laweyeseka.