You are here:CategoriesNkhani Zam'maboma
10
July

10/07/15

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 2163 times

Mfumu ithetsa banja kamba ka nsanje
Mfumu yina kwa Nsamala m’boma la Balaka lathetsa banja lake chifukwa cha msanje.

09
July

09/07/15

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 2050 times

Alandidwa phone kamba kowilikiza zibwenzi 

Mkulu wina kwa Kanduku mboma la Mwanza waona mbwadza mkazi wake atamulanda phone ya m’manja chifukwa chowirikiza zibwenzi.

08
July

08/07/15

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 2076 times

Wamisala azunguza mayi wina kamba kabuluku othina
Mayi wina pa malo okwelera bus yopita ku Mulanje waona ngati malodza wamisala atayamba kumuzazila ati kamba koti anavala buluku lothina.

07
July

07/07/15

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 1980 times

Omwalira azizitswa anthu ataoneka pagulu la anamfedwa
Mikoko yogona ya m’mudzi wina kwa Chilikumwendo mboma la Dedza maka mudzi omwe wayandikana ndiku Mitundu mboma la Lilongwe yaima mitu m’nyamata wina yemwe anamwalila atamuona ali patsogolo pagulu lomwe linanyamula malilo ake kupita kumanda.

About us

Malawi Broadcasting Corporation is a public broadcaster mandated and formed by Government under an Act of Parliament in 1964, to enhance the successful implementation of all its social and economic programs...

Social Media

Catch us on these social networks for more information

Facebook Twitter RSS

Get Your Newsletter