Aluma anthu kamba kosemphana maganizo
Mikoko yogona yapa mudzi wina kwa Nkalo mboma la Chiradzulu yadzudzula mkulu wina chifukwa choluma anthu angapo atasemphana maganizo.
Mwana wina aima pakhomo a manda
Anthu apa mudzi wina mboma la Neno aima mitu ndi zomwe anachita mwana wa Nyakwawa ina pokaima pakhomo kumanda ati kudikila chitanda cha bamboo ake.
Achilapa kuti sadzatukwananso
Mai wina wam’mudzi mwa Namalo ku Bangwe mu mzinda wa Blantyre wati wachimina sadzayambilanso kutukwana anzake m’mudzi bwalo litamulipitsa chindapusa cha 10-thousand Kwacha.
Awilikiza kuchita chibwenzi mamuna akuona
Mayi wina wa m’mudzi mwa Nicholas ku Ligowe mboma la Neno akudabwitsa anthu chifukwa chowirikiza kuchita chibwenzi ndi mphongo ina koma mwamuna wake osachitapo kanthu.