Chipwirikiti chinabuka pakati pa amai ena a gulu la banki nkhonde ku Machinjiri mu mzinda wa Blantyre.
Mnyamata wina ku Likuni m’boma la Lilongwe manja ali ku nkhongo mtsikana wina atamukwangwanula ndalama zake.
Mkulu wina wa udindo wake ku chipembedzo china kwa mfumu Maliri m’boma la Lilongwe waba ndalama za mpingo, njinga ya mkulu amene amayang’anira mpingowu mderali komanso mikanjo yomwe amavala akamapempheretsa.
Mtengwa wina mdera la Kacheche ku Mzimba ati sakumvetsa ndi zomwe zamuchitikira.