Athawa mamuna wa chibwenzi kamba ka ndalama
Tili mboma la Lilongwe m’mudzi mwa Kamwana, Mtsikana wina akuyenda mozemba poopa mwamuna wa chibwenzi yemwe anamudyera ndalama.
Mwambo wa chiliza usokonekela
Mwambo wachiliza unasokonekera nyakwawa zitakana kutsekula kumanda kwa gulupu Chonjowa mdera la Chilooko m’boma la Ntchisi.
Mwamuna wina asamuka kamba ka utambwali
Mwamuna wina mdera la Kachere ku Dedza wasamuka mderalo chifukwa cha utambwali.
Asambisidwa makofi kamba kau katakwe
Mwamuna wina kwa Ngokwe mboma la Machinga anaona zakuda anthu atamusambitsa ndi makofi chifukwa chozembetsa katundu.