Anthu atuluka mu mpingo
Anthu ambiri opemphera pa mpingo wina pa Neno Turn off mboma la Mwanza atuluka mu mpingowo chifukwa chaza khalidwe la mkazi wa mkulu wapa mpingowo.
Mai wina asowa mtendere kamba ka dama
Mai wina mdera la Nsamala ku Balaka akusowa mtendere chifukwa cha zomwe wachita. Maiyo yemwe mwamuna wake anapita ku Joni zaka zapitazo amakhala pa lendi mogundizana nyumba ndi banja lina.
Achilapa atagula nyama munjira
Mwamuna wina kwa Matenga m’boma la Ntchisi wanenetsa kuti sadzagulanso nyama iliyonse yongomutsatsa pa njira.
Alanda mkazi wa chimwene
Mnyamata wina ku Mitundu m’boma la Lilongwe walanda mkazi wa mchimwene wake m’boma la Salima.