Asonkheza ndalama za malipiro ake
Mikoko yogona kwa Nankhumba m’boma la Mangochi yapukusa mitu ndi zomwe wachita mkulu wina posokhetsa ndalama za malipilo ake chikhalilecho amalandila ndalama zina ku mabungwe komwe akugwira ntchito.
Mabanja asemphana kamba ka ufumu
Mabanja awiri achifumu kwa Santhe m’boma la Kasungu omwe ngapapachibale akukhalira kulalatilana tsiku liri lonse pa nkhani yaza ufumu.
Nyakwawa iimitsidwa udindo kamba ka nchiuno
Nyakwawa ina kwa Kaduya ku Phalombe ayamba ayimitsa pa udindo chifukwa chowilikiza khalidwe lake la mchuuno.
Ofulula mowa asatsa anthu
Omvera mau a Mulungu amalimbikitsa kuti tidzikhala opereka mcholinga choti tidzilandilanso zambiri, Koma nthawi zina mpofunika kusamala ndi zithandizo zina.