You are here:CategoriesNkhani Zam'maboma
12
May

12/05/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 5667 times

Asonkheza ndalama za malipiro ake 
Mikoko yogona kwa Nankhumba m’boma la Mangochi yapukusa mitu ndi zomwe wachita mkulu wina posokhetsa ndalama za malipilo ake chikhalilecho amalandila ndalama zina ku mabungwe komwe akugwira ntchito.

07
May

07/05/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 3098 times

Mabanja asemphana kamba ka ufumu

Mabanja awiri achifumu kwa Santhe m’boma la Kasungu omwe ngapapachibale akukhalira kulalatilana tsiku liri lonse pa nkhani yaza ufumu.

05
May

05/05/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 3375 times

Nyakwawa iimitsidwa udindo kamba ka nchiuno

Nyakwawa ina kwa Kaduya ku Phalombe ayamba ayimitsa pa udindo chifukwa chowilikiza khalidwe lake la mchuuno.

03
May

03/05/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 2797 times

Ofulula mowa asatsa anthu
Omvera mau a Mulungu amalimbikitsa kuti tidzikhala opereka mcholinga choti tidzilandilanso zambiri, Koma nthawi zina mpofunika kusamala ndi zithandizo zina.

About us

Malawi Broadcasting Corporation is a public broadcaster mandated and formed by Government under an Act of Parliament in 1964, to enhance the successful implementation of all its social and economic programs...

Social Media

Catch us on these social networks for more information

Facebook Twitter RSS

Get Your Newsletter