Malawi Broadcasting Corporation
Local Nkhani Sports

Flames wapsa waku Guinea

Timu ya mpira wamiyendo yadziko lino yanyamuka kupita m’dziko la Equatorial Guinea komwe akasewere ndi timu yadzikolo mumpikisano wodzigulira malo wapadziko lonse.

Timuyi ikagona ku Addis Ababa mdziko la Ethiopia ndipo idzapitiriza ulendo wawo waku Equatorial Guinea loweruka mmawa.

Timu ya Flames Ili panambala yachitatu mugulu H ndi mapointi asanu ndi imodzi.

Maulendo anayi omwe Malawi yakumana ndi Equatorial Guinea mumpikisano monga omwewu, Flames yapambana kamodzi, kufananitsa mphamvu kamodzi ndipo yagonja kawiri.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Muyembekezere ntchito zachitukuko zochuluka – Mia

Charles Pensulo

Namondwe Chido wakula mphamvu

Charles Pensulo

MEC to roll out pilot voter registration

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.