Malawi Broadcasting Corporation
Local Nkhani Sports

Flames wapsa waku Guinea

Timu ya mpira wamiyendo yadziko lino yanyamuka kupita m’dziko la Equatorial Guinea komwe akasewere ndi timu yadzikolo mumpikisano wodzigulira malo wapadziko lonse.

Timuyi ikagona ku Addis Ababa mdziko la Ethiopia ndipo idzapitiriza ulendo wawo waku Equatorial Guinea loweruka mmawa.

Timu ya Flames Ili panambala yachitatu mugulu H ndi mapointi asanu ndi imodzi.

Maulendo anayi omwe Malawi yakumana ndi Equatorial Guinea mumpikisano monga omwewu, Flames yapambana kamodzi, kufananitsa mphamvu kamodzi ndipo yagonja kawiri.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

MCCCI Business Leaders Summit receives boost from Britam Insurance

Alinafe Mlamba

Chakwera opens new KU Tobacco Commission House

MBC Online

Mlooka Solar-Powered Irrigation Scheme a blessing for Zomba — Water Users Association

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.