Malawi Broadcasting Corporation
Local Nkhani

Dekhani AMalawi zikutheka — Chakwera

Prezidenti wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, watsimikizira anthu a m’boma la Dowa kuti vuto la madzi likhala mbiri ya makedzana.

Poyankhula kwa khwimbi la anthu limene linasonkhana pa Madisi Trading Centre, Dr Chakwera wati kubwera kwa chitukuko cha madzi Cha Kholongo Multipurpose Dam zithandizira kwambiri kusintha miyoyo ya anthu a m’boma la Dowa ndi madela wozungulira.

Pa chifukwachi, mtsogoleri wa dziko linoyu wapempha aMalawi kuti adekhe pomwe akukhazikitsa zitukuko zosiyanasiyana mokomera aMalawi onse.

Chitukuko cha madzi cha Kholongo Multipurpose Dam chikuyembekeza kutha chaka cha mawa.

Print Friendly, PDF & Email

Author

  • Mayeso Chikhadzula joined MBC in 2006, he's an Investigative Journalist and Principal Reporter. He's also a News Anchor, Presenter, and producer.

Related posts

ACB, SOS on graft-busting drill

Jeffrey Chinawa

Chotsani katangale pa ndondomeko yothandiza anthu — DoDMA

MBC Online

Tipitiriza kuthandiza Malawi – IMF

Justin Mkweu
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.