Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

CHITUKUKO CHIFIKIRE MADERA ONSE — ZIKHALE

Mmodzi wa akulu akulu mchipani cha MCP yemwenso ndi nduna yaza Chitetezo Chadziko a Ken Zikhale Ng’oma ati boma lipitiriza kutukula madera onse a dziko lino mosakondera potukula miyoyo ya anthu.

Mwachitsanzo,iwo anakamba za ntchito ya minda ikulu ikulu ya Mega Farms imene ikugwiridwa ku Machinga.

A Zikhale Ng’oma amayankhula pa bwalo laza masewero la Chaka ku Machinga pa msonkhano omwe anachititsa.

Mu kanema ali m’musiyu, akuonetsa zina zomwe a Ng’oma analankhula.

#MBCOnlineServices

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Global outage plagues Facebook, sparks widespread disruption

Alinafe Mlamba

CHAKWERA CHALLENGES MDF SENIOR OFFICERS ON PROFESSIONALISM AND ETHICS

MBC Online

Public Pension Funds’ assets valued at K340 billion

Aisha Amidu
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.