Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

CHITUKUKO CHIFIKIRE MADERA ONSE — ZIKHALE

Mmodzi wa akulu akulu mchipani cha MCP yemwenso ndi nduna yaza Chitetezo Chadziko a Ken Zikhale Ng’oma ati boma lipitiriza kutukula madera onse a dziko lino mosakondera potukula miyoyo ya anthu.

Mwachitsanzo,iwo anakamba za ntchito ya minda ikulu ikulu ya Mega Farms imene ikugwiridwa ku Machinga.

A Zikhale Ng’oma amayankhula pa bwalo laza masewero la Chaka ku Machinga pa msonkhano omwe anachititsa.

Mu kanema ali m’musiyu, akuonetsa zina zomwe a Ng’oma analankhula.

#MBCOnlineServices

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Nkhanza za m’banja zachuluka m’boma la Balaka – Apolisi

MBC Online

KNH supports inclusive education with bus donation

MBC Online

Soldiers donate to Kamuzu Central Hospital

Doreen Sonani
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.