Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

Chakwera wanyamuka kubwelera ku Lilongwe

Mtsogoleri wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, wanyamuka m’chigawo chakummwera, kudzera pa bwalo la ndege la Chileka, kubwelera ku Lilongwe.

A Chakwera anali m’chigawo chakummwera pa Limbe Police Training School mumzinda wa Blantyre, kumene anatsogolera mwambo otulutsa apolisi omwe atsiriza maphunziro awo.

Nduna ya zofalitsa nkhani, a Moses Kunkuyu, nduna yoona za madzi ndi ukhondo, a Abida Mia, mafumu komanso atsogoleri andale ndi ena mwa anthu omwe anatsanzikana ndi Dr Chakwera komanso Madam Monica Chakwera pabwalo la ndege la Chileka.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Kale Langa yagwedeza Kaning’ina

MBC Online

Tonse titengepo gawo, atero a Chakwera

MBC Online

Malawi ndi bwenzi lenileni la dziko la Zambia — Lufuma

Mayeso Chikhadzula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.