Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

Chakwera wanyamuka kubwelera ku Lilongwe

Mtsogoleri wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, wanyamuka m’chigawo chakummwera, kudzera pa bwalo la ndege la Chileka, kubwelera ku Lilongwe.

A Chakwera anali m’chigawo chakummwera pa Limbe Police Training School mumzinda wa Blantyre, kumene anatsogolera mwambo otulutsa apolisi omwe atsiriza maphunziro awo.

Nduna ya zofalitsa nkhani, a Moses Kunkuyu, nduna yoona za madzi ndi ukhondo, a Abida Mia, mafumu komanso atsogoleri andale ndi ena mwa anthu omwe anatsanzikana ndi Dr Chakwera komanso Madam Monica Chakwera pabwalo la ndege la Chileka.

Related posts

Pali kusintha kwina pa programme — Kunkuyu

Rabson Kondowe

Apha makwacha ndi ulimi wamakono wa mpunga

Alinafe Mlamba

Abambo awiri awapeza olakwa pamulandu wosakaza nkhalango

Mayeso Chikhadzula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.