Malawi Broadcasting Corporation
Business Local News Nkhani

Chakumwa chaukali chatsopano!

Kampani yofulula mowa ya Castel, yakhazikitsa chakumwa chatsopano chimene akuchitcha kuti Pomme Breeze.

M’modzi mwa akuluakulu a kampaniyi, a Fiona Nyambo, ati chakumwa chaukali chimenechi ndi chozuna komanso chokonzedwa mwa makono.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Environmental NGO calls for stronger reforestation drive

McDonald Chiwayula

MACODA and EWF orient persons with disabilities on new Disability Act

MBC Online

Mpatsa Holdings procures 49% of MyBucks

Alick Sambo
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.