Malawi Broadcasting Corporation
Business Local News Nkhani

Chakumwa chaukali chatsopano!

Kampani yofulula mowa ya Castel, yakhazikitsa chakumwa chatsopano chimene akuchitcha kuti Pomme Breeze.

M’modzi mwa akuluakulu a kampaniyi, a Fiona Nyambo, ati chakumwa chaukali chimenechi ndi chozuna komanso chokonzedwa mwa makono.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Former Nkhoma Synod Secretary General inaugurated as Group Gusu

Paul Mlowoka

Bushiri agawa chakudya kwa okhudzidwa ndi njala ku Nkhotakota

Yamikani Simutowe

Norway, WFP sign MOU for $5.2million support towards El Niño response efforts

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.