Malawi Broadcasting Corporation
Business Local News Nkhani

Chakumwa chaukali chatsopano!

Kampani yofulula mowa ya Castel, yakhazikitsa chakumwa chatsopano chimene akuchitcha kuti Pomme Breeze.

M’modzi mwa akuluakulu a kampaniyi, a Fiona Nyambo, ati chakumwa chaukali chimenechi ndi chozuna komanso chokonzedwa mwa makono.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

‘Avoidable air pollution-induced deaths must trigger action’

MBC Online

ROYAL FAMILY GATHERS AT BALMORAL AMID CONCERNS FOR QUEEN’S HEALTH

MBC Online

17 women vie for councillorship, parliamentary seats in Rumphi

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.