Malawi Broadcasting Corporation
Business Local News Nkhani

Chakumwa chaukali chatsopano!

Kampani yofulula mowa ya Castel, yakhazikitsa chakumwa chatsopano chimene akuchitcha kuti Pomme Breeze.

M’modzi mwa akuluakulu a kampaniyi, a Fiona Nyambo, ati chakumwa chaukali chimenechi ndi chozuna komanso chokonzedwa mwa makono.

 

Related posts

Kineo & Aidfest to release debut EP

Romeo Umali

President Chakwera to respond SONA questions

Rabson Kondowe

Nkhonya ya Hannock Phiri ndi Regene Champion ikununkhira

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.