Malawi Broadcasting Corporation
Business Local News Nkhani

Chakumwa chaukali chatsopano!

Kampani yofulula mowa ya Castel, yakhazikitsa chakumwa chatsopano chimene akuchitcha kuti Pomme Breeze.

M’modzi mwa akuluakulu a kampaniyi, a Fiona Nyambo, ati chakumwa chaukali chimenechi ndi chozuna komanso chokonzedwa mwa makono.

 

Related posts

Livingstonia Synod mourns Chilima and eight others

Rabson Kondowe

Chilima, nine others killed in plane crash

Romeo Umali

NACALA LOGISTICS HIKES PASSENGER TRAIN PRICES

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.