Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

Boma la America lapereka K12BN ku boma la Malawi

Boma la United States, kudzera ku bungwe la USAID, lapereka K12 billion ku boma la Malawi kuti zithandizire anthu amene akhudzidwa ndi njala.

Polengeza za thandizoli, a Pamela Fessenden, omwe ndi mkulu wa USAID Malawi, ati izi zikutsatira kulengeza kwa mtsogoleri wa dziko lino Dr Lazarus Chakwera kuti maboma 23 mwa maboma 28 ali pa ngozi ya njala m’dziko muno.

Iwo ati apitiriza kuthandiza boma la Malawi mu njira zosiyanasiyana.

Olemba: Blessings Cheleuka

Related posts

SADC to discuss security situation in the region

Romeo Umali

President Chakwera arrives in Mulanje

Romeo Umali

Moroccan delegation engages Malawi Parliament on children’s rights

McDonald Chiwayula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.