Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

Anthu oposa 600 atuluka DPP ndikulowa MCP ku Mulanje

Anthu omwe anali mamembala a chipani cha DPP okwana 619 ochokera m’madera a kummwera komanso pakati m’boma la Mulanje, alengeza kuti atuluka chipanichi ndipo alowa Malawi Congress (MCP).

Mmodzi wa akuluakulu a MCP, a Brown Mpinganjira, Wapampando wa chipanichi ku Mulanje komanso wachiwiri kwa mkulu wa achinyamata mchipani cha MCP, a Blessings Chilembwe, ndiwo alandira anthuwa pamwambo umene unachitika pa Mulanje paboma.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

NGORA yati K1BN ithandiza mabungwe awo kudzidalira

Emmanuel Chikonso

“A Gotani – Hara ali ndi luntha potsogolera” — President Chakwera

Timothy Kateta

Ndondomeko ya zachuma ikupereka chiyembekezo – World Bank

Justin Mkweu
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.