Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani

Abusa apereka penti ku Polisi ya Chinsapo

Atsogoleri a mipingo ku Likuni ndi kwa Chinsapo ku Lilongwe apereka penti yokwana malita 35 ku Polisi ya Chinsapo Unit kuti akonzere denga limene liri ndi dzimbiri.

Mkulu wa Likuni and Chinsapo Pastors Fraternal, Reverend Daniel Masamba, anati zimakhala zomvetsa chisoni kuona apolisi akupulumutsa katundu wa nkhaninkhani kwambava koma kulephera kupulumutsa denga lawo.

Mkulu wa Polisiyi, a Mavuto Banda, anayamikira chifukwa cha mphatsozi.

M’mbuyomu, atsogoleri a mipingowa anabyzala mitengo pa Polisiyo kaamba kogwira bwino ntchito.

Olemba: Raymond Midaya

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Chimaneni laid to rest

MBC Online

Martyrs’ Day commemoration service of worship underway

MBC Online

Coolest’s ‘Degree’ sparks conversation!

Alinafe Mlamba
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.