Malawi Broadcasting Corporation
Health Local Local News Nkhani

Azimayi sakugwiritsa ntchito makondomu achizimayi

Zadziwika kuti amayi ambiri sakonda kugwiritsa ntchito makondomu achizimayi zomwe zikupangitsa kuti makondomu-wa adziwonongeka asanagwiritsidwe ntchito.

Wanena izi ndi mkulu owona zopewa kufala kwa kachirombo ka HIV wa bungwe la Aids Healthcare Foundation (AHF) kuchigawo chakum’mwera, a Jacob Pidini.

Iwo amafotokoza izi pamwambo wa tsiku lokumbukira kufunika kwa kondomu popewa kutenga mimba zosayembekezera, kutenga matenda opatsirana pogonana kuphatikizapo HIV.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Mumba wakhazikitsa mfundo zake

MBC Online

Police to deploy intelligence-driven operation

Chisomo Break

Boma lati dziko lino silikuchita bwino pankhani zaukhondo

Paul Mlowoka
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.