Malawi Broadcasting Corporation
Health Local Local News Nkhani

Azimayi sakugwiritsa ntchito makondomu achizimayi

Zadziwika kuti amayi ambiri sakonda kugwiritsa ntchito makondomu achizimayi zomwe zikupangitsa kuti makondomu-wa adziwonongeka asanagwiritsidwe ntchito.

Wanena izi ndi mkulu owona zopewa kufala kwa kachirombo ka HIV wa bungwe la Aids Healthcare Foundation (AHF) kuchigawo chakum’mwera, a Jacob Pidini.

Iwo amafotokoza izi pamwambo wa tsiku lokumbukira kufunika kwa kondomu popewa kutenga mimba zosayembekezera, kutenga matenda opatsirana pogonana kuphatikizapo HIV.

 

Related posts

Suspected mpox cases test negative

Alinafe Mlamba

Tipitiriza kuthandiza Malawi – IMF

Rabson Kondowe

‘Respect the rights of people with disabilities’

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.