Malawi Broadcasting Corporation
Health Local Local News Nkhani

Azimayi sakugwiritsa ntchito makondomu achizimayi

Zadziwika kuti amayi ambiri sakonda kugwiritsa ntchito makondomu achizimayi zomwe zikupangitsa kuti makondomu-wa adziwonongeka asanagwiritsidwe ntchito.

Wanena izi ndi mkulu owona zopewa kufala kwa kachirombo ka HIV wa bungwe la Aids Healthcare Foundation (AHF) kuchigawo chakum’mwera, a Jacob Pidini.

Iwo amafotokoza izi pamwambo wa tsiku lokumbukira kufunika kwa kondomu popewa kutenga mimba zosayembekezera, kutenga matenda opatsirana pogonana kuphatikizapo HIV.

 

Related posts

Students  fight against plastic pollution

McDonald Chiwayula

WORLD RADIO DAY: MISA MALAWI CALLS FOR IMPARTIAL REPORTING

Romeo Umali

Lilongwe businessman wins big in BetPawa’s aviator

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.