Malawi Broadcasting Corporation
Health Local Local News Nkhani

Azimayi sakugwiritsa ntchito makondomu achizimayi

Zadziwika kuti amayi ambiri sakonda kugwiritsa ntchito makondomu achizimayi zomwe zikupangitsa kuti makondomu-wa adziwonongeka asanagwiritsidwe ntchito.

Wanena izi ndi mkulu owona zopewa kufala kwa kachirombo ka HIV wa bungwe la Aids Healthcare Foundation (AHF) kuchigawo chakum’mwera, a Jacob Pidini.

Iwo amafotokoza izi pamwambo wa tsiku lokumbukira kufunika kwa kondomu popewa kutenga mimba zosayembekezera, kutenga matenda opatsirana pogonana kuphatikizapo HIV.

 

Related posts

World Vision Malawi commits to address health challenges

Alinafe Mlamba

NGORA yati K1BN ithandiza mabungwe awo kudzidalira

Romeo Umali

ECAMA’s 2024 Annual Economic Conference to address Malawi’s economic challenges

McDonald Chiwayula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.